Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 65:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Inu mumasamalira dziko lapansi,

      Mumalichititsa kuti libale zipatso zambiri* komanso kuti likhale lachonde.+

      Mtsinje wochokera kwa Mulungu ndi wodzadza ndi madzi.

      Mumachititsa kuti dziko lapansi lipereke chakudya kwa anthu,+

      Umu ndi mmene dziko lapansi munalipangira.

      10 Mumanyowetsa minda yake komanso kusalaza dothi limene lalimidwa,*

      Mumaifewetsa ndi mvula yamvumbi. Mumadalitsa zomera zake.+

  • Yeremiya 14:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kodi pa mafano opanda pake a mitundu ya anthu pali fano lililonse limene lingagwetse mvula?

      Kapena kodi kumwamba pakokha kungagwetse mvula yamvumbi?

      Kodi si inu nokha, Yehova Mulungu wathu, amene mumachititsa zimenezi?+

      Chiyembekezo chathu chili mwa inu

      Chifukwa inu nokha ndi amene mumachita zonsezi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena