-
Yeremiya 14:22Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
22 Kodi pa mafano opanda pake a mitundu ya anthu pali fano lililonse limene lingagwetse mvula?
Kapena kodi kumwamba pakokha kungagwetse mvula yamvumbi?
Kodi si inu nokha, Yehova Mulungu wathu, amene mumachititsa zimenezi?+
Chiyembekezo chathu chili mwa inu
Chifukwa inu nokha ndi amene mumachita zonsezi.
-