Salimo 15:1, 2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Inu Yehova, ndi ndani amene angakhale mlendo mutenti yanu? Ndi ndani amene angakhale mʼphiri lanu lopatulika?+ 2 Ndi amene akuyenda mosalakwitsa zinthu,*+Amene amachita zinthu zabwino+Komanso kulankhula zoona mumtima mwake.+ Salimo 24:3, 4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ndi ndani angakwere kuphiri la Yehova,+Ndipo ndi ndani angaime mʼmalo ake opatulika? 4 Aliyense amene ndi wosalakwa komanso wopanda chinyengo mumtima mwake,+Amene sanalumbire mwachinyengo potchula moyo Wanga,*Kapena kulumbira pofuna kupusitsa anthu ena.+ Salimo 25:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Anthu amene amaopa Yehova ndi amene amakhala naye pa ubwenzi wolimba,+Ndipo amawadziwitsa pangano lake.+
15 Inu Yehova, ndi ndani amene angakhale mlendo mutenti yanu? Ndi ndani amene angakhale mʼphiri lanu lopatulika?+ 2 Ndi amene akuyenda mosalakwitsa zinthu,*+Amene amachita zinthu zabwino+Komanso kulankhula zoona mumtima mwake.+
3 Ndi ndani angakwere kuphiri la Yehova,+Ndipo ndi ndani angaime mʼmalo ake opatulika? 4 Aliyense amene ndi wosalakwa komanso wopanda chinyengo mumtima mwake,+Amene sanalumbire mwachinyengo potchula moyo Wanga,*Kapena kulumbira pofuna kupusitsa anthu ena.+
14 Anthu amene amaopa Yehova ndi amene amakhala naye pa ubwenzi wolimba,+Ndipo amawadziwitsa pangano lake.+