1 Samueli 15:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Sauli anayankha Samueli kuti: “Komatu ndamvera+ mawu a Yehova, chifukwa ndachita ntchito imene Yehova anandituma, ndipo ndabweretsa Agagi,+ mfumu ya Amaleki. Koma Aamalekiwo ndawapha.+ Esitere 3:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pambuyo pake, Mfumu Ahasiwero analemekeza Hamani+ mwana wa Hamedata Mwagagi,+ ndipo anam’kweza+ ndi kum’patsa mpando wapamwamba kuposa akalonga ena onse amene mfumuyo inali nawo.+ Esitere 7:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Choncho anapachika Hamani pamtengo+ umene anakonzera Moredekai,+ ndipo mkwiyo wa mfumu unatha. Esitere 9:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Izi zinali choncho chifukwa Hamani+ mwana wa Hamedata+ Mwagagi,+ amene anali kudana+ ndi Ayuda onse, anakonzera Ayudawo chiwembu kuti awawononge.+ Choncho iye anachita Puri+ kapena kuti Maere,+ ndi cholinga chakuti awasautse ndi kuwawononga.
20 Sauli anayankha Samueli kuti: “Komatu ndamvera+ mawu a Yehova, chifukwa ndachita ntchito imene Yehova anandituma, ndipo ndabweretsa Agagi,+ mfumu ya Amaleki. Koma Aamalekiwo ndawapha.+
3 Pambuyo pake, Mfumu Ahasiwero analemekeza Hamani+ mwana wa Hamedata Mwagagi,+ ndipo anam’kweza+ ndi kum’patsa mpando wapamwamba kuposa akalonga ena onse amene mfumuyo inali nawo.+
24 Izi zinali choncho chifukwa Hamani+ mwana wa Hamedata+ Mwagagi,+ amene anali kudana+ ndi Ayuda onse, anakonzera Ayudawo chiwembu kuti awawononge.+ Choncho iye anachita Puri+ kapena kuti Maere,+ ndi cholinga chakuti awasautse ndi kuwawononga.