Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 26:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ndidzasamba m’manja mwanga kusonyeza kuti ndine wopanda cholakwa,+

      Ndipo ndidzayenda mozungulira guwa lanu lansembe, inu Yehova,+

  • Yeremiya 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsuka mtima wako ndi kuchotsa zoipa zonse, iwe Yerusalemu, kuti upulumuke.+ Kodi maganizo ako oipawo udzakhala nawo mpaka liti?+

  • Machitidwe 22:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Nanga ukuchedweranji? Nyamuka, ubatizidwe+ ndi kusamba+ kuti uchotse machimo ako mwa kuitana pa dzina lake.’+

  • Chivumbulutso 7:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Nthawi yomweyo, ndinamuyankha kuti: “Mbuyanga, mukudziwa ndinu.” Ndipo iye anati: “Amenewa ndi amene atuluka m’chisautso chachikulu,+ ndipo achapa mikanjo yawo ndi kuiyeretsa+ m’magazi+ a Mwanawankhosa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena