Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 13
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 13:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 18:22; Yer 6:13; Eze 13:2; Zek 13:4
  • +Yer 23:25; 27:9
  • +Mko 13:22; 2At 2:9

Deuteronomo 13:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 28:9; Mt 7:22

Deuteronomo 13:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 8:19
  • +De 8:2; Sl 66:10; Mt 24:24; 1Ak 11:19; 2At 2:11
  • +De 6:5; 10:12; Mt 22:37

Deuteronomo 13:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 10:20

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/15/2002, ptsa. 16-17

Deuteronomo 13:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 9:15
  • +De 18:20; Yer 14:14; Zek 13:3
  • +De 6:14
  • +De 17:7; 1Ak 5:13

Deuteronomo 13:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 18:1
  • +1Mf 11:4; 2Pe 2:1

Deuteronomo 13:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 1:10; Aga 1:8
  • +Eze 9:5

Deuteronomo 13:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 22:20; 32:27; Nu 25:5
  • +De 17:7

Deuteronomo 13:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 20:2, 27; De 17:5
  • +Eks 13:3

Deuteronomo 13:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 17:13; 19:20; 1Ti 1:20; 5:20

Deuteronomo 13:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 2:12; 1Mf 21:10; Yuda 19
  • +2Mf 17:21

Deuteronomo 13:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 17:4; 19:15; 1Ti 5:19; Ahe 10:28

Deuteronomo 13:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mb 28:6
  • +Eks 22:20; Le 27:28

Deuteronomo 13:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 6:24
  • +Yos 8:28; Yer 49:2; Mik 1:6

Deuteronomo 13:17

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu akuti “kanthu kalikonse koyenera kuwonongedwa” angalembedwenso kuti “kanthu kalikonse kotembereredwa.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 6:18; 7:1
  • +Yos 7:26; 22:20
  • +Eks 33:19; Sl 78:38
  • +Ge 22:17; 26:4; 28:14

Deuteronomo 13:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 12:32; Ne 1:5; Sl 119:4; 1Yo 5:3
  • +Eks 15:26; De 6:18

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 13:1De 18:22; Yer 6:13; Eze 13:2; Zek 13:4
Deut. 13:1Yer 23:25; 27:9
Deut. 13:1Mko 13:22; 2At 2:9
Deut. 13:2Yer 28:9; Mt 7:22
Deut. 13:3Yes 8:19
Deut. 13:3De 8:2; Sl 66:10; Mt 24:24; 1Ak 11:19; 2At 2:11
Deut. 13:3De 6:5; 10:12; Mt 22:37
Deut. 13:4De 10:20
Deut. 13:5Yes 9:15
Deut. 13:5De 18:20; Yer 14:14; Zek 13:3
Deut. 13:5De 6:14
Deut. 13:5De 17:7; 1Ak 5:13
Deut. 13:61Sa 18:1
Deut. 13:61Mf 11:4; 2Pe 2:1
Deut. 13:8Miy 1:10; Aga 1:8
Deut. 13:8Eze 9:5
Deut. 13:9Eks 22:20; 32:27; Nu 25:5
Deut. 13:9De 17:7
Deut. 13:10Le 20:2, 27; De 17:5
Deut. 13:10Eks 13:3
Deut. 13:11De 17:13; 19:20; 1Ti 1:20; 5:20
Deut. 13:131Sa 2:12; 1Mf 21:10; Yuda 19
Deut. 13:132Mf 17:21
Deut. 13:14De 17:4; 19:15; 1Ti 5:19; Ahe 10:28
Deut. 13:152Mb 28:6
Deut. 13:15Eks 22:20; Le 27:28
Deut. 13:16Yos 6:24
Deut. 13:16Yos 8:28; Yer 49:2; Mik 1:6
Deut. 13:17Yos 6:18; 7:1
Deut. 13:17Yos 7:26; 22:20
Deut. 13:17Eks 33:19; Sl 78:38
Deut. 13:17Ge 22:17; 26:4; 28:14
Deut. 13:18De 12:32; Ne 1:5; Sl 119:4; 1Yo 5:3
Deut. 13:18Eks 15:26; De 6:18
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 13:1-18

Deuteronomo

13 “Mneneri+ kapena wolota maloto+ akauka pakati panu n’kukupatsani chizindikiro kapena chodabwitsa cholosera zam’tsogolo,+ 2 ndipo chizindikiro kapena chodabwitsa chimenecho chachitikadi,+ chimene anachita ponena kuti, ‘Tiyeni titsatire milungu ina imene simunaidziwe, ndipo tiitumikire,’ 3 musamvere mawu a mneneriyo kapena wolotayo,+ chifukwa Yehova Mulungu wanu akukuyesani+ kuti adziwe ngati mukukonda Yehova Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse.+ 4 Muzitsatira Yehova Mulungu wanu, muzimuopa, muzisunga malamulo ake, muzimvera mawu ake, muzim’tumikira ndi kum’mamatira.+ 5 Ndipo mneneri+ kapena wolota malotoyo muzimupha,+ chifukwa walankhula mopandukira Yehova Mulungu wanu amene anakutulutsani m’dziko la Iguputo ndi kukuwombolani m’nyumba yaukapolo. Munthu ameneyo walankhula zimenezo kuti akupatutseni panjira imene Yehova Mulungu wanu anakulamulani kuyendamo.+ Choncho muzichotsa woipayo pakati panu.+

6 “M’bale wako, amene ndi mwana wamwamuna wa mayi ako, kapena mwana wako wamwamuna, mwana wako wamkazi, mkazi wako wokondedwa kapena bwenzi lako lapamtima,+ akayesa kukupatutsa mwamseri pokuuza kuti, ‘Tiye tikatumikire milungu ina,’+ milungu imene iwe kapena makolo ako sanaidziwe, 7 milungu ina mwa milungu ya anthu okuzungulirani, okhala pafupi nanu kapena okhala kutali, kuchokera kumalekezero ena a dziko kukafika kumalekezero ena, 8 usavomereze zofuna zake kapena kumumvera.+ Diso lako lisamumvere chifundo ndipo usamumvere chisoni+ kapena kum’bisa kuti um’teteze. 9 Koma umuphe ndithu.+ Dzanja lako lizikhala loyamba kum’ponya miyala kuti afe, ndipo anthu ena onse azibwera pambuyo.+ 10 Uzim’ponya miyala kuti afe,+ chifukwa anali kufuna kukupatutsa ndi kukuchotsa kwa Yehova Mulungu wako, amene anakutulutsa m’dziko la Iguputo, m’nyumba yaukapolo.+ 11 Pamenepo Aisiraeli onse adzamva ndi kuchita mantha, ndipo sadzachita chinthu choipa chilichonse chofanana ndi chimenechi pakati panu.+

12 “Mu umodzi mwa mizinda yanu, imene Yehova Mulungu wanu wakupatsani kuti mukhalemo, mukadzamva kuti, 13 ‘Pakati panu papezeka anthu opanda pake+ amene akufuna kupatutsa anthu mumzinda wawo,+ ponena kuti: “Tiyeni tikatumikire milungu ina,” milungu imene inu simunaidziwe,’ 14 muzifunafuna, kufufuza ndi kufunsitsa za nkhani imeneyo.+ Mukapeza kuti ndi zoonadi, choipa chimenechi chachitikadi pakati panu, 15 muzipha ndithu anthu a mumzindawo ndi lupanga.+ Muziwononga+ ndi lupanga mzindawo ndi chilichonse chimene chili mmenemo, kuphatikizapo ziweto zake. 16 Zofunkha zake zonse muzizisonkhanitsa pakati pa bwalo la mzindawo. Pamenepo muzitentha mzindawo+ ndi zofunkha zake zonse monga nsembe yathunthu yoperekedwa kwa Yehova Mulungu wanu. Ndipo mzindawo uzikhala bwinja mpaka kalekale.+ Usadzamangidwenso. 17 Ndipo kanthu kalikonse koyenera kuwonongedwa* kasamamatire kudzanja lanu,+ kuti mkwiyo woyaka moto wa Yehova usiye kukuyakirani+ ndipo akuchitireni chifundo ndi kukumverani chisoni,+ kutinso akuchulukitseni, monga mmene analumbirira makolo anu.+ 18 Motero muzimvera mawu a Yehova Mulungu wanu, mwa kusunga malamulo ake+ onse amene ndikukupatsani lero, kuti muzichita zinthu zoyenera pamaso pa Yehova Mulungu wanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena