Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 18:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Kunena za ana a Levi, iwo ndawapatsa chakhumi+ chilichonse mu Isiraeli monga cholowa chawo chifukwa cha utumiki wawo umene akuchita, utumiki wa pachihema chokumanako.

  • Deuteronomo 14:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Mlevi wokhala mumzinda wanu usamutaye,+ pakuti alibe gawo kapena cholowa monga iwe.+

  • 2 Mbiri 31:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kuwonjezera pamenepo, Hezekiya anauza anthu okhala mu Yerusalemu kuti apereke gawo loyenera kupita kwa ansembe+ ndi Alevi,+ n’cholinga choti iwo azitsatira+ mosamala chilamulo cha Yehova.+

  • Nehemiya 10:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Wansembe, mwana wamwamuna wa Aroni, azikhala ndi Alevi pamene iwo akulandira chakhumi.* Aleviwo azipereka gawo limodzi mwa magawo 10 a chakhumicho kunyumba ya Mulungu+ wathu kuzipinda zodyera+ m’nyumba yosungiramo zinthu.

  • Malaki 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Kodi munthu wochokera kufumbi angabere Mulungu? Komatu inu mukundibera.”

      Inu mukunena kuti: “Takuberani motani?”

      “Mukundibera kudzera m’chakhumi* ndi m’zopereka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena