Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 33
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 33:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:28; Lu 24:50
  • +Yos 14:6; Sl 90:kam

Deuteronomo 33:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:18
  • +Owe 5:4
  • +Hab 3:3
  • +Da 7:10; Aga 3:19; Yuda 14
  • +Sl 68:17

Deuteronomo 33:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 7:8; 23:5; Sl 47:4; Ho 11:1
  • +Eks 19:6; Sl 50:5
  • +Eks 19:23
  • +Eks 20:19

Deuteronomo 33:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 24:8; Yoh 1:17; Mac 15:5; 1Ak 9:9
  • +De 4:8; Mac 7:53

Deuteronomo 33:5

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani mawu a m’munsi pa De 32:15.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 32:15; Yes 44:2
  • +Eks 18:25; 19:7; Nu 1:44
  • +Nu 1:46

Deuteronomo 33:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:3; Yos 22:1; 1Mb 5:1
  • +Nu 26:7; Yos 13:15

Deuteronomo 33:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:8; 1Mb 5:2
  • +Sl 78:68
  • +Owe 1:2; 2Sa 7:1, 9

Deuteronomo 33:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:5; Nu 3:12; 18:24
  • +Eks 28:30; Le 8:8; Eza 2:63
  • +Eks 32:26; Ahe 7:26
  • +Eks 17:7; De 6:16
  • +Nu 20:13

Deuteronomo 33:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:27; Le 10:6
  • +Le 10:7
  • +Mki 2:5

Deuteronomo 33:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 10:11; De 17:9; Yer 18:18
  • +2Mb 15:3; 17:9; Mki 2:7
  • +Eks 30:7; Nu 16:40
  • +Le 1:9; Sl 51:19

Deuteronomo 33:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 18:32; Yes 40:29; Hab 3:19; Afi 4:13
  • +De 18:5; Mki 2:6
  • +Mac 23:4
  • +Sl 3:7; Amo 5:10

Deuteronomo 33:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:27
  • +2Sa 7:16
  • +Sl 4:8
  • +Yos 18:11; Sl 68:27
  • +Yos 18:28; Owe 1:21; 2Sa 5:9; Sl 125:2

Deuteronomo 33:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:22
  • +Yos 16:1; Miy 10:22
  • +Ge 27:28; Zek 8:12
  • +Ge 49:25

Deuteronomo 33:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Sa 23:4
  • +Le 26:5; Sl 65:9

Deuteronomo 33:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 37:25; Yos 17:18

Deuteronomo 33:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 8:8; Sl 24:1
  • +Eks 3:4; Mac 7:30
  • +Ge 49:26; 1Mb 5:1
  • +Ge 37:7; 1Mb 5:2

Deuteronomo 33:17

Mawu a M'munsi

  • *

    Mwina nyama imeneyi inali yooneka ngati njati.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 17:1
  • +Sl 22:21; 92:10
  • +1Mf 22:11; Sl 44:5
  • +Ge 48:19

Deuteronomo 33:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:13
  • +Yos 19:10; Owe 5:14
  • +Ge 49:14; Yos 19:17

Deuteronomo 33:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 4:5
  • +Ge 49:13; Mt 4:13

Deuteronomo 33:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:19
  • +Yos 13:8, 24
  • +1Mb 12:8; Miy 28:1
  • +1Mb 5:18, 20

Deuteronomo 33:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 32:1
  • +Nu 32:21, 27, 33; Yos 1:14, 15; 4:12; 22:1

Deuteronomo 33:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:16
  • +Owe 13:2, 24; 15:8, 20; 16:30
  • +Yos 19:47; Owe 18:27, 29; 1Mb 12:35

Deuteronomo 33:23

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:21
  • +Yos 19:32

Deuteronomo 33:24

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:20
  • +Sl 127:3; 128:3
  • +Miy 3:4
  • +De 32:13; Yob 29:6

Deuteronomo 33:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 8:9

Deuteronomo 33:26

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 15:11; Sl 86:8; 89:6; Yer 10:6
  • +De 32:15; 33:5; Yes 44:2
  • +Sl 68:33
  • +Sl 68:34; 93:1; 104:3

Deuteronomo 33:27

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 46:11; 90:1; 91:2; 125:2
  • +Yes 40:11; Ho 11:3
  • +De 9:3
  • +De 31:4

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    11/2021, ptsa. 6-7

    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu,

    9/2021, tsa. 2

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/1991, tsa. 13

Deuteronomo 33:28

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 23:6; 33:16
  • +Sl 68:26; Yes 48:1
  • +De 8:8
  • +De 11:11; 33:13

Deuteronomo 33:29

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 33:12; 144:15; 146:5
  • +De 4:7; 2Sa 7:23; Sl 147:20
  • +Sl 27:1; Yes 12:2
  • +Ge 15:1; Sl 115:9
  • +Owe 7:20
  • +2Sa 22:45; Sl 66:3; 81:15
  • +De 32:13

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 33:1Ge 49:28; Lu 24:50
Deut. 33:1Yos 14:6; Sl 90:kam
Deut. 33:2Eks 19:18
Deut. 33:2Owe 5:4
Deut. 33:2Hab 3:3
Deut. 33:2Da 7:10; Aga 3:19; Yuda 14
Deut. 33:2Sl 68:17
Deut. 33:3De 7:8; 23:5; Sl 47:4; Ho 11:1
Deut. 33:3Eks 19:6; Sl 50:5
Deut. 33:3Eks 19:23
Deut. 33:3Eks 20:19
Deut. 33:4Eks 24:8; Yoh 1:17; Mac 15:5; 1Ak 9:9
Deut. 33:4De 4:8; Mac 7:53
Deut. 33:5De 32:15; Yes 44:2
Deut. 33:5Eks 18:25; 19:7; Nu 1:44
Deut. 33:5Nu 1:46
Deut. 33:6Ge 49:3; Yos 22:1; 1Mb 5:1
Deut. 33:6Nu 26:7; Yos 13:15
Deut. 33:7Ge 49:8; 1Mb 5:2
Deut. 33:7Sl 78:68
Deut. 33:7Owe 1:2; 2Sa 7:1, 9
Deut. 33:8Ge 49:5; Nu 3:12; 18:24
Deut. 33:8Eks 28:30; Le 8:8; Eza 2:63
Deut. 33:8Eks 32:26; Ahe 7:26
Deut. 33:8Eks 17:7; De 6:16
Deut. 33:8Nu 20:13
Deut. 33:9Eks 32:27; Le 10:6
Deut. 33:9Le 10:7
Deut. 33:9Mki 2:5
Deut. 33:10Le 10:11; De 17:9; Yer 18:18
Deut. 33:102Mb 15:3; 17:9; Mki 2:7
Deut. 33:10Eks 30:7; Nu 16:40
Deut. 33:10Le 1:9; Sl 51:19
Deut. 33:11Sl 18:32; Yes 40:29; Hab 3:19; Afi 4:13
Deut. 33:11De 18:5; Mki 2:6
Deut. 33:11Mac 23:4
Deut. 33:11Sl 3:7; Amo 5:10
Deut. 33:12Ge 49:27
Deut. 33:122Sa 7:16
Deut. 33:12Sl 4:8
Deut. 33:12Yos 18:11; Sl 68:27
Deut. 33:12Yos 18:28; Owe 1:21; 2Sa 5:9; Sl 125:2
Deut. 33:13Ge 49:22
Deut. 33:13Yos 16:1; Miy 10:22
Deut. 33:13Ge 27:28; Zek 8:12
Deut. 33:13Ge 49:25
Deut. 33:142Sa 23:4
Deut. 33:14Le 26:5; Sl 65:9
Deut. 33:15Ge 37:25; Yos 17:18
Deut. 33:16De 8:8; Sl 24:1
Deut. 33:16Eks 3:4; Mac 7:30
Deut. 33:16Ge 49:26; 1Mb 5:1
Deut. 33:16Ge 37:7; 1Mb 5:2
Deut. 33:17Yos 17:1
Deut. 33:17Sl 22:21; 92:10
Deut. 33:171Mf 22:11; Sl 44:5
Deut. 33:17Ge 48:19
Deut. 33:18Ge 49:13
Deut. 33:18Yos 19:10; Owe 5:14
Deut. 33:18Ge 49:14; Yos 19:17
Deut. 33:19Sl 4:5
Deut. 33:19Ge 49:13; Mt 4:13
Deut. 33:20Ge 49:19
Deut. 33:20Yos 13:8, 24
Deut. 33:201Mb 12:8; Miy 28:1
Deut. 33:201Mb 5:18, 20
Deut. 33:21Nu 32:1
Deut. 33:21Nu 32:21, 27, 33; Yos 1:14, 15; 4:12; 22:1
Deut. 33:22Ge 49:16
Deut. 33:22Owe 13:2, 24; 15:8, 20; 16:30
Deut. 33:22Yos 19:47; Owe 18:27, 29; 1Mb 12:35
Deut. 33:23Ge 49:21
Deut. 33:23Yos 19:32
Deut. 33:24Ge 49:20
Deut. 33:24Sl 127:3; 128:3
Deut. 33:24Miy 3:4
Deut. 33:24De 32:13; Yob 29:6
Deut. 33:25De 8:9
Deut. 33:26Eks 15:11; Sl 86:8; 89:6; Yer 10:6
Deut. 33:26De 32:15; 33:5; Yes 44:2
Deut. 33:26Sl 68:33
Deut. 33:26Sl 68:34; 93:1; 104:3
Deut. 33:27Sl 46:11; 90:1; 91:2; 125:2
Deut. 33:27Yes 40:11; Ho 11:3
Deut. 33:27De 9:3
Deut. 33:27De 31:4
Deut. 33:28Yer 23:6; 33:16
Deut. 33:28Sl 68:26; Yes 48:1
Deut. 33:28De 8:8
Deut. 33:28De 11:11; 33:13
Deut. 33:29Sl 33:12; 144:15; 146:5
Deut. 33:29De 4:7; 2Sa 7:23; Sl 147:20
Deut. 33:29Sl 27:1; Yes 12:2
Deut. 33:29Ge 15:1; Sl 115:9
Deut. 33:29Owe 7:20
Deut. 33:292Sa 22:45; Sl 66:3; 81:15
Deut. 33:29De 32:13
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
  • 26
  • 27
  • 28
  • 29
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 33:1-29

Deuteronomo

33 Tsopano ili ndi dalitso+ limene Mose, munthu wa Mulungu woona,+ anadalitsa nalo ana a Isiraeli iye asanafe. 2 Ndipo anati:

“Yehova anafika kuchokera ku Sinai,+

Anathwanima pa iwo kuchokera ku Seiri.+

Anawala kuchokera kudera lamapiri la Parana,+

Ndipo anali ndi miyandamiyanda ya oyera ake,+

Kudzanja lake lamanja kunali ankhondo ake.+

 3 Iye analinso kukonda anthu ake.+

Oyera awo onse ali m’manja mwanu.+

Iwowa anakhala pansi, pamapazi panu.+

Anayamba kulandira ena mwa mawu anu.+

 4 (Mose anatipatsa chilamulo,+

Chimene mpingo wa Yakobo uli nacho monga chawo.)+

 5 Mulungu anakhala mfumu mu Yesuruni,*+

Pamene atsogoleri a anthu anasonkhana pamodzi,+

Chiwerengero chonse cha mafuko a Isiraeli.+

 6 Rubeni akhale ndi moyo, asafe ayi,+

Ndipo anthu ake asakhale ochepa.”+

7 Popitiriza, iye anapereka dalitso lotsatirali kwa Yuda,+ kuti:

“Inu Yehova, imvani mawu a Yuda,+

M’bweretseni kwa anthu ake.

Manja ake amenya nkhondo pofuna kulanditsa zinthu zake.

Mukhaletu mthandizi wake kwa adani ake.”+

8 Ndipo kwa Levi anati:+

“Tumimu ndi Urimu+ wanu ndizo za munthu wokhulupirika kwa inu,+

Amene munamuyesa pa Masa.+

Munayamba kulimbana naye pafupi ndi madzi a Meriba.+

 9 Munthu amene anauza bambo ndi mayi ake kuti, ‘Sindinawaone.’

Ngakhale abale ake sanawavomereze,+

Ndipo ana ake sanawadziwe.

Pakuti anasunga mawu anu,+

Ndipo anapitiriza kusunga pangano lanu.+

10 Amenewa azilangiza Yakobo pa zigamulo zanu,+

Ndi Isiraeli m’chilamulo chanu.+

Azipereka nsembe zofukiza kuti muzinunkhiza fungo lake,+

Ndi nsembe yathunthu paguwa lanu lansembe.+

11 Inu Yehova dalitsani mphamvu zake,+

Ndipo mukondwere ndi ntchito ya manja ake.+

Muvulaze koopsa ziuno za amene akumuukira,+

Ndi amene amadana naye kwambiri, kuti asamuukire.”+

12 Kwa Benjamini anati:+

“Wokondedwa+ wa Yehova akhale m’chitetezo cha Mulungu,+

Pamene akumutchinjiriza tsiku lonse,+

Ndipo iye akhale pakati pa mapewa ake.”+

13 Ndipo kwa Yosefe anati:+

“Dziko lake lipitirize kudalitsidwa ndi Yehova.+

Lidalitsidwe ndi zinthu zabwino kwambiri zakumwamba, mame,+

Ndi madzi akuya a pansi pa nthaka.+

14 Lidalitsidwenso ndi zinthu zabwino kwambiri, zochokera ku dzuwa,+

Ndi zinthu zabwino kwambiri, zokolola za miyezi yosiyanasiyana,+

15 Lidalitsidwe ndi zinthu zabwino koposa, za m’mapiri a kum’mawa,+

Ndi zinthu zabwino kwambiri za m’mapiri amene adzakhalapo mpaka kalekale.

16 Lidalitsidwe ndi zinthu zabwino kwambiri za padziko lapansi, ndi chuma chake chonse,+

Komanso movomerezedwa ndi Iye amene anaonekera m’chitsamba chaminga.+

Zimenezi zikhale pamutu pa Yosefe,+

Paliwombo pa munthu wopatulidwa pakati pa abale ake.+

17 Ulemerero wake ndi wofanana ndi wa mwana wa ng’ombe wamphongo woyamba kubadwa,+

Ndipo nyanga zake ndi nyanga za ng’ombe yam’tchire yamphongo.*+

Nyanga zimenezo adzakankha nazo anthu.+

Adzakankha nazo anthu onse pamodzi mpaka kukafika kumalekezero a dziko lapansi.

Nyanga zimenezo ndi anthu masauzande makumimakumi a fuko la Efuraimu,+

Ndiponso anthu masauzande a fuko la Manase.”

18 Kwa Zebuloni anati:+

“Kondwera Zebuloni iwe, pa maulendo ako,+

Ndiponso iwe Isakara, m’mahema ako.+

19 Adzaitanira mitundu ya anthu kuphiri.

Kumeneko adzapereka nsembe zachilungamo.+

Pakuti adzayamwa chuma chochuluka cha m’nyanja,+

Ndi chuma chobisika cha mumchenga.”

20 Ndipo kwa Gadi anati:+

“Wodala ndi iye wofutukula malire a dera la Gadi.+

Iye adzakhala ngati mkango,+

Ndipo adzakhadzula dzanja, adzang’amba mutu paliwombo.+

21 Adzatenga gawo labwino kwambiri kukhala lake,+

Pakuti gawo loperekedwa ndi wopereka malamulo linasungidwa kumeneko.+

Ndipo atsogoleri a anthu adzasonkhana.

Iye adzachitadi chilungamo cha Yehova,

Ndi zigamulo zokhudza Isiraeli.”

22 Kwa Dani anati:+

“Dani ndi mwana wa mkango.+

Adzadumpha kuchokera ku Basana.”+

23 Ndipo kwa Nafitali anati:+

“Nafitali wakhutira chifukwa chovomerezedwa ndi Yehova,

Ndipo madalitso Ake amuchulukira.

Tenga chigawo cha kumadzulo ndi kum’mwera.”+

24 Kwa Aseri anati:+

“Aseri ndi wodalitsidwa ndi ana aamuna.+

Akhale wovomerezeka ndi abale ake,+

Woponda phazi lake m’mafuta.+

25 Chitsulo ndi mkuwa ndizo zokhomera chipata chako,+

Udzayenda mtima uli phee, masiku onse a moyo wako.

26 Palibe wina wofanana ndi Mulungu woona+ wa Yesuruni,+

Amene amayenda m’mlengalenga pokuthandiza,+

Amene amayenda pamitambo mu ulemerero wake.+

27 Mulungu wakale lomwe ndiwo malo ako obisalamo,+

Ndipo iwe uli m’manja amene adzakhalapo mpaka kalekale.+

Adzapitikitsa mdani pamaso pako,+

Ndipo adzanena kuti, ‘Awononge!’+

28 Isiraeli adzakhala motetezeka,+

Kasupe wa Yakobo adzakhala mosatekeseka,+

M’dziko lokhala ndi chakudya ndi vinyo watsopano.+

Ndipo kumwamba kwake kudzagwetsa mame.+

29 Ndiwe wodala Isiraeli iwe!+

Ndani angafanane ndi iwe,+

Anthu amene akupulumutsidwa ndi Yehova,+

Chishango chako chokuthandiza,+

Amenenso ndi lupanga lako lopambana?+

Adani ako adzakhala mwamantha chifukwa cha iwe,+

Ndipo iwe udzayendayenda pamalo awo okwezeka.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena