Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 23
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 23:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 56:4; Mt 19:12
  • +Le 21:20

Deuteronomo 23:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 20:14; Le 20:10; Yoh 8:41; Ahe 12:8

Deuteronomo 23:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ne 13:1

Deuteronomo 23:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 25:45
  • +De 2:29; Owe 11:18
  • +Nu 22:6; Yos 24:9; Ne 13:2

Deuteronomo 23:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 22:35; Mik 6:5
  • +Nu 23:11, 25; 24:10; Sl 3:8
  • +De 7:7; 33:3; Eze 16:8; Mki 1:2

Deuteronomo 23:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Sa 8:2; 12:31

Deuteronomo 23:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 25:24; 36:1; Nu 20:14; Ob 10
  • +Ge 15:13; 46:6; Eks 22:21; Le 19:34; Sl 105:23

Deuteronomo 23:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 21:5; 2Sa 11:11

Deuteronomo 23:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 15:16
  • +1Sa 20:26

Deuteronomo 23:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 15:31

Deuteronomo 23:12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/1/2012, tsa. 6

    Chinsinsi cha Banja, ptsa. 46-47

Deuteronomo 23:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 24:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/1/2012, tsa. 6

    Chinsinsi cha Banja, ptsa. 46-47

    Galamukani!,

    12/8/1991, tsa. 22

Deuteronomo 23:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:12
  • +De 7:2, 23
  • +1Pe 1:16
  • +Le 26:17; 2Pe 3:14

Deuteronomo 23:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 30:15

Deuteronomo 23:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 16:3
  • +Eks 22:21; Yer 7:5; Zek 7:9; Mki 3:5

Deuteronomo 23:17

Mawu a M'munsi

  • *

    Kutanthauza mnyamata wosungidwira kugonedwa ndi amuna.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 19:29; 21:9
  • +1Mf 14:24; 15:12; 2Mf 23:7

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/1997, tsa. 29

    4/15/1989, tsa. 3

Deuteronomo 23:18

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu awa angatanthauze munthu amene makamaka amagona mnyamata kumbuyo.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eze 16:33
  • +Ge 19:5; Aro 1:27; 1Ti 1:10; Chv 22:15

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/1997, tsa. 29

    4/15/1989, tsa. 3

Deuteronomo 23:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 22:25; Le 25:36; Ne 5:10; Sl 15:5; Eze 18:8; 22:12
  • +Le 25:37

Deuteronomo 23:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 15:6
  • +Miy 28:8; Eze 18:17
  • +De 15:4, 10; Miy 19:17; Lu 6:35

Deuteronomo 23:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Owe 11:30; 1Sa 1:11
  • +Yob 22:27; Sl 66:13; 116:18; Mla 5:4; Yon 2:9; Nah 1:15
  • +Mla 5:6; Aro 1:31; Yak 4:17

Deuteronomo 23:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mla 5:5

Deuteronomo 23:23

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 30:2; Sl 15:4; Miy 20:25
  • +Owe 11:35; 1Sa 14:24; Mt 5:33

Deuteronomo 23:24

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 6:11; Aro 13:10

Deuteronomo 23:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 12:1; Lu 6:1

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 23:1Yes 56:4; Mt 19:12
Deut. 23:1Le 21:20
Deut. 23:2Eks 20:14; Le 20:10; Yoh 8:41; Ahe 12:8
Deut. 23:3Ne 13:1
Deut. 23:4Mt 25:45
Deut. 23:4De 2:29; Owe 11:18
Deut. 23:4Nu 22:6; Yos 24:9; Ne 13:2
Deut. 23:5Nu 22:35; Mik 6:5
Deut. 23:5Nu 23:11, 25; 24:10; Sl 3:8
Deut. 23:5De 7:7; 33:3; Eze 16:8; Mki 1:2
Deut. 23:62Sa 8:2; 12:31
Deut. 23:7Ge 25:24; 36:1; Nu 20:14; Ob 10
Deut. 23:7Ge 15:13; 46:6; Eks 22:21; Le 19:34; Sl 105:23
Deut. 23:91Sa 21:5; 2Sa 11:11
Deut. 23:10Le 15:16
Deut. 23:101Sa 20:26
Deut. 23:11Le 15:31
Deut. 23:131Sa 24:3
Deut. 23:14Le 26:12
Deut. 23:14De 7:2, 23
Deut. 23:141Pe 1:16
Deut. 23:14Le 26:17; 2Pe 3:14
Deut. 23:151Sa 30:15
Deut. 23:16Yes 16:3
Deut. 23:16Eks 22:21; Yer 7:5; Zek 7:9; Mki 3:5
Deut. 23:17Le 19:29; 21:9
Deut. 23:171Mf 14:24; 15:12; 2Mf 23:7
Deut. 23:18Eze 16:33
Deut. 23:18Ge 19:5; Aro 1:27; 1Ti 1:10; Chv 22:15
Deut. 23:19Eks 22:25; Le 25:36; Ne 5:10; Sl 15:5; Eze 18:8; 22:12
Deut. 23:19Le 25:37
Deut. 23:20De 15:6
Deut. 23:20Miy 28:8; Eze 18:17
Deut. 23:20De 15:4, 10; Miy 19:17; Lu 6:35
Deut. 23:21Owe 11:30; 1Sa 1:11
Deut. 23:21Yob 22:27; Sl 66:13; 116:18; Mla 5:4; Yon 2:9; Nah 1:15
Deut. 23:21Mla 5:6; Aro 1:31; Yak 4:17
Deut. 23:22Mla 5:5
Deut. 23:23Nu 30:2; Sl 15:4; Miy 20:25
Deut. 23:23Owe 11:35; 1Sa 14:24; Mt 5:33
Deut. 23:24Mt 6:11; Aro 13:10
Deut. 23:25Mt 12:1; Lu 6:1
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 23:1-25

Deuteronomo

23 “Mwamuna wofulidwa+ mwa kuphwanya mavalo+ ake kapena woduka maliseche asalowe mumpingo wa Yehova.

2 “Mwana wapathengo+ asalowe mumpingo wa Yehova. Ana ake asalowe mumpingo wa Yehova kufikira m’badwo wa 10.

3 “Muamoni kapena Mmowabu asalowe mumpingo wa Yehova.+ Ana awo asalowe mumpingo wa Yehova kufikira m’badwo wa 10, ngakhalenso mpaka kalekale. 4 Chifukwa chake n’chakuti, sanakuthandizeni+ ndi mkate ndi madzi pamene munali pa ulendo mutatuluka mu Iguputo,+ ndiponso chifukwa chakuti analemba ganyu Balamu mwana wa Beori, amene kwawo ndi ku Petori ku Mesopotamiya kuti akutemberereni.+ 5 Yehova Mulungu wanu sanafune kumvera Balamu,+ m’malomwake Yehova Mulungu wanu anakusinthirani temberero kukhala dalitso,+ chifukwa Yehova Mulungu wanu anakukondani.+ 6 Musachite kanthu kowathandiza kupeza mtendere ndi chitukuko masiku onse a moyo wanu, mpaka kalekale.+

7 “Usaipidwe ndi Mwedomu, chifukwa ndi m’bale wako.+

“Usaipidwe ndi Mwiguputo, chifukwa unali mlendo m’dziko lawo.+ 8 Ana awo a m’badwo wachitatu angalowe mumpingo wa Yehova.

9 “Ukamanga msasa kuti umenyane ndi adani ako, uzidzipatula ku choipa chilichonse.+ 10 Pakati panu pakakhala mwamuna amene sali woyera chifukwa cha chodetsa chochitika usiku,+ azipita kunja kwa msasa. Asalowe mumsasamo.+ 11 Madzulo asambe ndipo dzuwa likalowa angathe kulowa mumsasa.+ 12 Muzikhala ndi malo obisika kunja kwa msasa kumene muzipita. 13 Uzikhalanso ndi chokumbira pamodzi ndi zida zako. Ndiyeno podzithandiza kunja kwa msasa, uzikumba dzenje ndi chokumbiracho ndipo ukamaliza kudzithandiza uzitembenuka ndi kufotsera zoipazo.+ 14 Pakuti Yehova Mulungu wanu akuyendayenda mumsasa wanu kuti akulanditseni+ ndi kupereka adani anu m’manja mwanu.+ Choncho msasa wanu uzikhala woyera,+ kuti asaone choipa chilichonse pakati panu ndi kutembenuka n’kuleka kuyenda nanu limodzi.+

15 “Kapolo akathawira kwa iwe kuchokera kwa mbuye wake, usam’bweze kwa mbuye wakeyo.+ 16 Apitirize kukhala ndi iwe pakati panu, pamalo alionse amene iye angasankhe mu umodzi mwa mizinda yanu,+ kulikonse kumene wakonda. Usamamuzunze.+

17 “Mwana wamkazi aliyense wachiisiraeli asakhale hule wa pakachisi,+ ndiponso mwana wamwamuna aliyense wachiisiraeli asakhale hule wa pakachisi.*+ 18 Usabweretse malipiro+ a hule kapena malipiro a galu*+ m’nyumba ya Yehova Mulungu wako kuti ukwaniritse lonjezo lililonse, chifukwa zonsezo ndi zonyansa kwa Yehova Mulungu wako.

19 “M’bale wako usamulipiritse chiwongoladzanja+ pa ndalama, chakudya+ kapena chilichonse chimene munthu angafunepo chiwongoladzanja. 20 Mlendo+ ungamulipiritse chiwongoladzanja, koma m’bale wako usamulipiritse chiwongoladzanja,+ kuti Yehova Mulungu wako akudalitse pa zochita zako zonse m’dziko limene ukupita kukalitenga kukhala lako.+

21 “Ukapereka lonjezo kwa Yehova+ Mulungu wako usachedwe kulikwaniritsa kuopera kuti ungachimwe,+ chifukwa Yehova Mulungu wako adzafuna ndithu kuti ukwaniritse chimene walonjezacho.+ 22 Koma ukapanda kulonjeza, sunachimwe.+ 23 Uzisunga mawu a pakamwa pako+ ndipo uzikwaniritsa lonjezo limene unapereka kwa Yehova Mulungu wako monga nsembe yaufulu. Uzichita zimenezi chifukwa unalonjeza ndi pakamwa pako.+

24 “Ukapita m’munda wa mpesa wa mnzako uzidya mphesa kungoti ukhute pa nthawiyo, koma usaike zina m’chotengera chako.+

25 “Ukalowa m’munda wa tirigu wa mnzako, uzipulula ndi dzanja lako tirigu yekhayo amene wacha, koma usamwete tirigu wa mnzako ndi chikwakwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena