Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Akorinto 10
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

2 Akorinto 10:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 11:29
  • +Mt 11:30
  • +1Ak 2:3
  • +2Ak 10:10

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    4/1/2003, tsa. 24

    8/1/1994, ptsa. 15-16

2 Akorinto 10:2

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu ake enieni, “mwakuthupi.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ak 4:21; 2Ak 13:2, 10

2 Akorinto 10:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aga 2:20
  • +Aro 8:13; Aef 6:12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kukambitsirana, ptsa. 369-370

2 Akorinto 10:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 26:52; Aro 13:12; Aef 6:13; 1At 5:8; 1Ti 1:18; 2Ti 2:24
  • +Aro 8:14; 2Ak 6:7

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    9/2016, ptsa. 8-9

    Nsanja ya Olonda,

    2/15/2010, ptsa. 12-13

    9/15/2009, tsa. 22

    10/1/1999, ptsa. 11-12

    2/1/1994, tsa. 12

    Kukambitsirana, ptsa. 369-370

2 Akorinto 10:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ak 1:19; 3:19; 2Ti 2:25

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    6/2019, ptsa. 8-13

    Nsanja ya Olonda,

    8/15/2013, tsa. 27

    2/15/2010, ptsa. 12-13

    10/1/1999, ptsa. 11-12

    2/1/1994, tsa. 12

    2/1/1987, tsa. 23

    Galamukani!,

    6/8/1994, tsa. 17

2 Akorinto 10:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ti 1:20; Ahe 12:10
  • +2Ak 2:9; 7:15

2 Akorinto 10:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ak 5:12
  • +1Yo 4:6

2 Akorinto 10:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ak 12:6
  • +2Ak 13:10; Ahe 13:17

2 Akorinto 10:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ak 10:1; Aga 4:13
  • +2Ak 11:6

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/15/2000, tsa. 13

    11/15/1996, tsa. 13

2 Akorinto 10:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ak 12:20; 13:2

2 Akorinto 10:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ak 3:1; 5:12
  • +Miy 25:27; 26:12; Aga 6:3, 4

2 Akorinto 10:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 12:3
  • +Mac 9:15; Aga 2:8

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    7/15/2008, tsa. 28

2 Akorinto 10:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ak 3:10; 4:15

2 Akorinto 10:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 15:20
  • +2At 1:3
  • +1Ak 9:1

2 Akorinto 10:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 19:21; Aro 15:24

2 Akorinto 10:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 65:16; Yer 9:24; 1Ak 1:31

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Galamukani!,

    7/8/1999, tsa. 27

2 Akorinto 10:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Lu 18:14
  • +1Sa 13:14; Miy 29:26
  • +Aro 2:29; 1Ak 4:5; 2Ti 2:15

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

2 Akor. 10:1Mt 11:29
2 Akor. 10:1Mt 11:30
2 Akor. 10:11Ak 2:3
2 Akor. 10:12Ak 10:10
2 Akor. 10:21Ak 4:21; 2Ak 13:2, 10
2 Akor. 10:3Aga 2:20
2 Akor. 10:3Aro 8:13; Aef 6:12
2 Akor. 10:4Mt 26:52; Aro 13:12; Aef 6:13; 1At 5:8; 1Ti 1:18; 2Ti 2:24
2 Akor. 10:4Aro 8:14; 2Ak 6:7
2 Akor. 10:51Ak 1:19; 3:19; 2Ti 2:25
2 Akor. 10:61Ti 1:20; Ahe 12:10
2 Akor. 10:62Ak 2:9; 7:15
2 Akor. 10:72Ak 5:12
2 Akor. 10:71Yo 4:6
2 Akor. 10:82Ak 12:6
2 Akor. 10:82Ak 13:10; Ahe 13:17
2 Akor. 10:102Ak 10:1; Aga 4:13
2 Akor. 10:102Ak 11:6
2 Akor. 10:112Ak 12:20; 13:2
2 Akor. 10:122Ak 3:1; 5:12
2 Akor. 10:12Miy 25:27; 26:12; Aga 6:3, 4
2 Akor. 10:13Aro 12:3
2 Akor. 10:13Mac 9:15; Aga 2:8
2 Akor. 10:141Ak 3:10; 4:15
2 Akor. 10:15Aro 15:20
2 Akor. 10:152At 1:3
2 Akor. 10:151Ak 9:1
2 Akor. 10:16Mac 19:21; Aro 15:24
2 Akor. 10:17Yes 65:16; Yer 9:24; 1Ak 1:31
2 Akor. 10:18Lu 18:14
2 Akor. 10:181Sa 13:14; Miy 29:26
2 Akor. 10:18Aro 2:29; 1Ak 4:5; 2Ti 2:15
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
2 Akorinto 10:1-18

2 Akorinto

10 Tsopano ineyo Paulo, ndikukudandaulirani mwa kufatsa+ ndi kukoma mtima+ kwa Khristu, ngakhale kuti ndimaoneka wosanunkha kanthu+ ndikakhala pakati panu, koma wolimba mtima polankhula nanu ndili kwina.+ 2 Ndithu ndikanakonda kuti anthu amene akuona kuti ifeyo timachita zinthu motsatira maganizo a dzikoli,* asinthe maganizo awo, kuti ndikadzabwera kumeneko ndisadzachite zinthu zazikulu zotsutsana nawo.+ 3 Pakuti ngakhale kuti moyo wathu ndi wofanana ndi wa anthu ena onse,+ sitikumenya nkhondo motsatira maganizo a dzikoli.+ 4 Pakuti zida za nkhondo yathu si zochokera m’dziko lino,+ koma ndi zida zamphamvu zimene Mulungu watipatsa,+ zimene zimatha kugwetsa zinthu zozikika molimba. 5 Pakuti tikugubuduza maganizo komanso chotchinga chilichonse chotsutsana ndi kudziwa Mulungu,+ ndipo tikugonjetsa ganizo lililonse n’kulimanga ngati mkaidi kuti lizimvera Khristu. 6 Komanso ndife okonzeka kupereka chilango pa aliyense wosamvera,+ inuyo mukadzasonyeza kuti ndinu omvera pa chilichonse.+

7 Mukuona zinthu mogwirizana ndi maonekedwe ake akunja.+ Ngati aliyense amakhulupirira mumtima mwake kuti ndi wotsatira Khristu, adziwenso kuti, monga mmene iye alili wotsatira Khristu, ifenso ndife otsatira Khristu.+ 8 Pakuti ngakhale nditati ndidzitamandire+ mopitirirako muyezo za ulamuliro umene Ambuye anatipatsa kuti tikulimbikitseni, osati kukupasulani,+ sindingachite manyazi. 9 Ponena zimenezi, sindikufuna kuti muganize kuti makalata anga cholinga chake n’kukuopsezani. 10 Pakuti ena amati: “Makalata ake ndi olemerera ndi amphamvu, koma iyeyo akakhala pakati pathu amaoneka wofooka+ ndipo nkhani zake n’zosagwira mtima.”+ 11 Munthu woteroyo adziwe kuti zimene tikunena m’makalata athu tili kwina, tidzachitanso zomwezo tikadzakhala pakati panu.+ 12 Pakuti sitidzayesa n’komwe kudziona ngati ndife ofanana ndi anthu enaake kapena kudziyerekezera ndi ena amene amadzikweza.+ Ndithudi anthu amenewo samvetsa kanthu kalikonse chifukwa akuyezana okhaokha pogwiritsira ntchito miyezo yawo yomwe, ndipo akudziyerekezera ndi iwo eni.+

13 Koma ifeyo tidzadzitamandira, osati pa zinthu zimene zili kunja kwa malire amene tapatsidwa,+ koma pa zinthu zimene zili mkati mwa malire a gawo limene Mulungu anatipatsa pochita kutiyezera, limene analifikitsa mpaka kwanuko.+ 14 Choncho sitikupitirira malire a gawo lathu, ngati kuti gawolo silikufika kwa inu. Ayi ndithu, pakuti tinayamba ndife kufika kwanuko polengeza uthenga wabwino wonena za Khristu.+ 15 Sitikudzitamandira kunja kwa malire a gawo limene tinapatsidwa, podzitamandira chifukwa cha ntchito za munthu wina ayi,+ koma tili ndi chiyembekezo chakuti chikhulupiriro chanu chikadzawonjezeka,+ ntchito yathunso idzakula pakati panu, limene ndi gawo lathu.+ Ndiyeno tidzachitanso zowonjezereka, 16 polengeza uthenga wabwino kumayiko akutali kupitirira kwanuko,+ kuti tisadzitamande m’gawo la wina, mmene anakonzamo kale. 17 “Koma amene akudzitamandira, adzitamande mwa Yehova.”+ 18 Pakuti wodzikweza yekha si amene amavomerezedwa,+ koma amene Yehova+ wamuvomereza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena