Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nyimbo ya Solomo 1
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Nyimbo ya Solomo 1:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 15:1; De 31:19; Owe 5:1; 2Sa 22:1; Sl 18:kam; Yes 5:1; Chv 15:3
  • +1Mf 4:32

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    11/15/2006, tsa. 17

Nyimbo ya Solomo 1:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 8:1
  • +Nym 4:10

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/2015, ptsa. 30-31

    11/15/2006, tsa. 18

    11/15/1987, tsa. 24

Nyimbo ya Solomo 1:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 27:9; Mla 9:8; Nym 5:5; Lu 23:56
  • +Mla 7:1

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/2015, ptsa. 30-31

    11/15/2006, tsa. 18

    11/15/1987, tsa. 24

Nyimbo ya Solomo 1:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yoh 6:44
  • +1Mf 7:1
  • +Yoh 15:13
  • +Mt 10:37

Nyimbo ya Solomo 1:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 45:9
  • +Sl 120:5; Eze 27:21
  • +Eks 36:14

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    11/15/2006, tsa. 18

Nyimbo ya Solomo 1:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 8:12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/2015, tsa. 32

    Galamukani!,

    4/8/1994, ptsa. 24-25

Nyimbo ya Solomo 1:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 18:20; Yes 5:1
  • +Nym 6:3; Yoh 10:11; Chv 7:17

Nyimbo ya Solomo 1:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 45:9; Aef 5:27

Nyimbo ya Solomo 1:9

Mawu a M'munsi

  • *

    Ena amati “hosi,” kapena “kavalo.”

  • *

    Onani Matanthauzo a Mawu Ena.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 6:4
  • +1Mf 10:28

Nyimbo ya Solomo 1:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eze 16:11

Nyimbo ya Solomo 1:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Sa 1:24; Yer 4:30

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    11/15/1987, tsa. 24

Nyimbo ya Solomo 1:12

Mawu a M'munsi

  • *

    Chimenechi ndi chitsamba chinachake chonunkhira bwino.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 4:13
  • +Yoh 12:3

Nyimbo ya Solomo 1:13

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani Matanthauzo a Mawu Ena.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 30:23; Est 2:12; Sl 45:8; Nym 4:6; 5:13; Yoh 19:39
  • +Nym 4:5

Nyimbo ya Solomo 1:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 4:13
  • +Yos 15:62

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    11/1/1989, tsa. 17

Nyimbo ya Solomo 1:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 45:11; Nym 4:7
  • +Ge 29:17; Nym 4:1; 5:2

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    11/15/2006, tsa. 18

Nyimbo ya Solomo 1:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 45:2; Nym 5:10; Yoh 1:14; Ahe 11:23
  • +Yob 7:13; Sl 132:3

Nyimbo ya Solomo 1:17

Mawu a M'munsi

  • *

    Ena amati “tsindwi.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 92:12; Yes 9:10

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Nyimbo 1:1Eks 15:1; De 31:19; Owe 5:1; 2Sa 22:1; Sl 18:kam; Yes 5:1; Chv 15:3
Nyimbo 1:11Mf 4:32
Nyimbo 1:2Nym 8:1
Nyimbo 1:2Nym 4:10
Nyimbo 1:3Miy 27:9; Mla 9:8; Nym 5:5; Lu 23:56
Nyimbo 1:3Mla 7:1
Nyimbo 1:4Yoh 6:44
Nyimbo 1:41Mf 7:1
Nyimbo 1:4Yoh 15:13
Nyimbo 1:4Mt 10:37
Nyimbo 1:5Sl 45:9
Nyimbo 1:5Sl 120:5; Eze 27:21
Nyimbo 1:5Eks 36:14
Nyimbo 1:6Nym 8:12
Nyimbo 1:71Sa 18:20; Yes 5:1
Nyimbo 1:7Nym 6:3; Yoh 10:11; Chv 7:17
Nyimbo 1:8Sl 45:9; Aef 5:27
Nyimbo 1:9Nym 6:4
Nyimbo 1:91Mf 10:28
Nyimbo 1:10Eze 16:11
Nyimbo 1:112Sa 1:24; Yer 4:30
Nyimbo 1:12Nym 4:13
Nyimbo 1:12Yoh 12:3
Nyimbo 1:13Eks 30:23; Est 2:12; Sl 45:8; Nym 4:6; 5:13; Yoh 19:39
Nyimbo 1:13Nym 4:5
Nyimbo 1:14Nym 4:13
Nyimbo 1:14Yos 15:62
Nyimbo 1:15Sl 45:11; Nym 4:7
Nyimbo 1:15Ge 29:17; Nym 4:1; 5:2
Nyimbo 1:16Sl 45:2; Nym 5:10; Yoh 1:14; Ahe 11:23
Nyimbo 1:16Yob 7:13; Sl 132:3
Nyimbo 1:17Sl 92:12; Yes 9:10
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Nyimbo ya Solomo 1:1-17

Nyimbo ya Solomo

1 Nyimbo yokoma kwambiri,+ nyimbo ya Solomo:+ 2 “Undipsompsone ndi milomo yako,+ chifukwa chikondi chimene umandisonyeza chimaposa vinyo kukoma kwake.+ 3 Mafuta+ ako odzola ndi onunkhira bwino. Dzina lako lili ngati mafuta othira pamutu.+ N’chifukwa chake atsikana amakukonda. 4 Nditenge,+ tiye tithawe! Chifukwatu mfumu yandipititsa m’zipinda zake zamkati.+ Tiye tikondwere ndi kusangalalira limodzi. Tiye tinene za chikondi chimene umandisonyeza osati za vinyo.+ M’pake kuti atsikana amakukonda.+

5 “Inu ana aakazi a ku Yerusalemu,+ ine ndine mtsikana wakuda ngati mahema a ku Kedara,+ koma wokongola ngati nsalu za mahema+ a Solomo. 6 Musandiyang’anitsitse chifukwa chakuti ndada, ndi dzuwatu landidetsali. Pakuti ana aamuna a mayi anga anandikwiyira. Choncho anandiika kuti ndiziyang’anira minda ya mpesa moti sindinathe kuyang’anira munda wangawanga wa mpesa.+

7 “Iwe amene mtima wanga umakukonda,+ tandiuza kumene umakadyetsera ziweto,+ kumene umakagonetsa ziweto masana. Kodi ndikhalirenji ngati mkazi amene wafunda nsalu ya namalira pakati pa magulu a ziweto za anzako?”

8 “Ngati iweyo sukudziwa, iwe mkazi wokongola kwambiri kuposa akazi onse,+ tsatira mapazi a ziweto ndipo ukadyetse ana ako a mbuzi pafupi ndi mahema a abusa.”

9 “Kwa ine, wokondedwa wangawe+ ndiwe wokongola ngati hatchi* yaikazi ya pamagaleta* a Farao.+ 10 Masaya ako ndi okongola pakati pa tsitsi lako lomanga, ndipo khosi lako lovala mkandalo limaoneka bwino.+ 11 Ife tikupangira zokongoletsa zoti uzivala kumutu. Zokongoletsazo zikhala zozungulira, zagolide,+ zokhala ndi mikanda yasiliva.”

12 “Pamene mfumu yakhala patebulo lake lozungulira, fungo labwino la nado*+ wanga likumveka kwa wokondedwa wanga.+ 13 Wachikondi wanga ali ngati kathumba ka mule*+ kwa ine. Iye adzakhala pakati pa mabere anga+ usiku wonse. 14 Kwa ine, wachikondi wanga ali ngati duwa lofiirira+ m’minda ya mpesa ya ku Eni-gedi.”+

15 “Ndiwe wokongola kwabasi, wokondedwa wanga.+ Ndiwe chiphadzuwa. Maso ako ali ngati maso a njiwa.”+

16 “Iwenso ndiwe wokongola,+ wachikondi wanga. Ndiwe mnyamata wosangalatsa kwambiri. Bedi+ lathunso ndi la masamba ofewa. 17 Nyumba yathu yokongola inamangidwa ndi mitengo ya mkungudza,+ ndipo kudenga* kwake kuli mitengo yofanana ndi mkungudza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena